| Malawis Hymne wurde geschrieben und komponiert von Michael-Fredrick Paul Sauka und ist seit der Unabhängigkeit im Jahre 1964 in Gebrauch. |
|
|
||||
| Text in Chichewa | Englische Übersetzung | |||
| Mlungu
dalitsani Malawi, Mumsunge m'mtendere. Gonjetsani adani onse, Njala, nthenda, nsanje. Lunzitsani mitima yathu, Kuti tisaope. Mdalitse Mtsogo leri nafe, Ndi Mai Malawi. |
O
God bless our land of Malawi, Keep it a land of peace. Put down each and every enemy, Hunger, disease, envy. Join together all our hearts as one, That we be free from fear. Bless our leader, each and every one, And Mother Malawi. |
|||
| Malawi ndziko
lokongola, La chonde ndi ufulu, Nyanja ndi mphepo ya m'mapiri, Ndithudi tadala. Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu, N'mphatso zaulere. Nkhalango, madambo abwino. Ngwokoma Malawi. |
Our own Malawi,
this land so fair, Fertile and brave and free. With its lakes, refreshing mountain air, How greatly blest are we. Hills and valleys, soil so rich and rare Give us a bounty free. Wood and forest, plains so broad and fair, All - beauteous Malawi. |
|||
| O Ufulu
tigwirizane, Kukweza Malawi. Ndi chikondi, khama, kumvera, Timutumikire. Pa nkhondo nkana pa mtendere, Cholinga n'chimodzi. Mai, bambo, tidzipereke, Pokweza Malawi. |
Freedom ever, let
us all unite To build up Malawi. With our love, our zeal and loyalty, Bringing our best to her. In time of war, or in time of peace, One purpose and one goal. Men and women serving selflessly In building Malawi. |
| Home |
Weiter |